Pomwe phungu wa nyumba ya malamulo ku m’mawa kwa boma la Rumphi a Kamlepo Kalua watulutsidwa pa belo lero, apolisi amangaso m’busa wa mpingo wa CCAP pamlandu okhudza kufalitsa za ngozi ya ndege yomwe inapha wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino a Saulos Chilima ndi anthu asanu ndi atatu.
DE LA MEME SOURCE
FAM Districts Leagues Launch Saturday [Malawi 24]
27 juin 2024
UTM Councillor elected Mzuzu City Mayor [Malawi 24]
26 juin 2024